Masalimo 110:6 - Buku Lopatulika6 Adzaweruza mwa amitundu, adzadzaza dziko ndi mitembo; adzaphwanya mitu m'maiko ambiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Adzaweruza mwa amitundu, adzadzaza dziko ndi mitembo; adzaphwanya mitu m'maiko ambiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Adzalanga mitundu ya anthu akunja, adzadzaza dziko lapansi ndi mitembo. Adzagonjetsa olamulira a pa dziko lonse lapansi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Adzaweruza anthu a mitundu ina, adzadzaza dziko lapansi ndi mitembo ndipo adzaphwanya olamulira a pa dziko lonse lapansi. Onani mutuwo |