Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 109:8 - Buku Lopatulika

8 Masiku ake akhale owerengeka; wina alandire udindo wake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Masiku ake akhale owerengeka; wina alandire udindo wake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Masiku ake akhale oŵerengeka, wina alandire udindo wake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Masiku ake akhale owerengeka; munthu wina atenge malo ake a utsogoleri.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 109:8
3 Mawu Ofanana  

Koma Inu, Mulungu, mudzawatsitsira kudzenje la chionongeko. Anthu okhetsa mwazi ndi achinyengo masiku ao sadzafikira nusu; koma ine ndidzakhulupirira Inu.


Ndipo iye anataya pansi ndalamazo pa Kachisi, nachokapo, nadzipachika yekha pakhosi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa