Masalimo 109:7 - Buku Lopatulika7 Ponenedwa mlandu wake atuluke wotsutsika; ndi pemphero lake likhale ngati kuchimwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ponenedwa mlandu wake atuluke wotsutsika; ndi pemphero lake likhale ngati kuchimwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Pomuweruza apezeke kuti ali ndi mlandu, mapemphero ake akhale ngati kupalamula. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Pamene aweruzidwa, apezeke kuti ndi wolakwa, ndipo mapemphero ake amutsutse. Onani mutuwo |