Masalimo 109:6 - Buku Lopatulika6 Muike munthu woipa akhale mkulu wake; ndi mdani aime padzanja lamanja lake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Muike munthu woipa akhale mkulu wake; ndi mdani aime pa dzanja lamanja lake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Sankhulani munthu woipa kuti aweruze mlandu wa wondiwukirayo, iye aimbidwe mlandu ndi munthu woneneza anzake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Sankhani munthu woyipa kuti amutsutse iye; lolani wotsutsa ayime ku dzanja lake lamanja. Onani mutuwo |