Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 109:30 - Buku Lopatulika

30 Ndidzayamika Yehova kwakukulu pakamwa panga; ndi pakati pa anthu aunyinji ndidzamlemekeza.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

30 Ndidzayamika Yehova kwakukulu pakamwa panga; ndi pakati pa anthu aunyinji ndidzamlemekeza.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

30 Ndidzathokoza Chauta kwambiri polankhula. Ndidzamtamanda pakati pa gulu la anthu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

30 Ndi pakamwa panga ndidzathokoza Yehova kwambiri; ndidzamutamanda mʼgulu lalikulu la anthu.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 109:30
12 Mawu Ofanana  

Amkwezenso mu msonkhano wa anthu, namlemekeze pokhala akulu.


Aleluya. Ndidzayamika Yehova ndi mtima wonse, mu upo wa oongoka mtima, ndi mumsonkhano.


Ndidzakuyamikani ndi mtima wanga wonse; ndidzaimba zakukulemekezani patsogolo pa milungu.


Mafumu onse a padziko lapansi adzakuyamikani, Yehova, popeza adamva mau a pakamwa panu.


Ndidzakuyamikani mu msonkhano waukulu; m'chikhamu cha anthu ndidzakulemekezani.


Ndidzayamika Yehova monga mwa chilungamo chake; ndipo ndidzaimbira Yehova Wam'mwambamwamba.


Ndidzayamika Yehova ndi mtima wanga wonse; ndidzawerengera zodabwitsa zanu zonse.


Ndi kuti, Ndidzalalikira dzina lanu kwa abale anga, pakati pa Mpingo ndidzakuimbirani.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa