Masalimo 109:31 - Buku Lopatulika31 Popeza adzaima padzanja lamanja la waumphawi, kumpulumutsa kwa iwo akuweruza koipa moyo wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 Popeza adzaima pa dzanja lamanja la waumphawi, kumpulumutsa kwa iwo akuweruza koipa moyo wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 Paja Chauta amaimirira pafupi ndi munthu wosoŵa, amafuna kumpulumutsa kwa anthu ogamula kuti iyeyo aphedwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Popeza Iye amayima ku dzanja lamanja la munthu wosowayo, kupulumutsa moyo wake kwa iwo amene agamula molakwa. Onani mutuwo |