Masalimo 109:29 - Buku Lopatulika29 Otsutsana nane avale manyazi, nadzikute nacho chisokonezo chao ngati ndi chofunda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Otsutsana nane avale manyazi, nadzikute nacho chisokonezo chao ngati ndi chofunda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Ondineneza akhale onyozeka, manyazi ao aŵakute ngati chovala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Onditsutsa adzavekedwa mnyozo, ndipo adzadzifunditsa manyazi ngati chovala. Onani mutuwo |