Masalimo 109:26 - Buku Lopatulika26 Ndithandizeni Yehova, Mulungu wanga: Ndipulumutseni monga mwa chifundo chanu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Ndithandizeni Yehova, Mulungu wanga: Ndipulumutseni monga mwa chifundo chanu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Thandizeni Chauta, Mulungu wanga. Pulumutseni chifukwa cha chikondi chanu chosasinthika. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Thandizeni Inu Yehova Mulungu wanga; pulumutseni molingana ndi chikondi chanu. Onani mutuwo |