Masalimo 109:25 - Buku Lopatulika25 Ndiwakhaliranso chotonza; pakundiona apukusa mutu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Ndiwakhaliranso chotonza; pakundiona apukusa mutu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Ondineneza amandinyodola, akandiwona amapukusa mitu yao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Ndine chinthu chotonzedwa kwa otsutsana nane; akandiona, amapukusa mitu yawo. Onani mutuwo |