Masalimo 109:27 - Buku Lopatulika27 kuti adziwe kuti ichi ndi dzanja lanu; kuti Inu Yehova munachichita. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 kuti adziwe kuti ichi ndi dzanja lanu; kuti Inu Yehova munachichita. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Adani adziŵe kuti limeneli ndi dzanja lanu londipulumutsa, Inu Chauta, ndinu amene mwachita zimenezi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Adaniwo adziwe kuti limeneli ndi dzanja lanu, kuti Inu Yehova mwachita zimenezi. Onani mutuwo |