Masalimo 109:23 - Buku Lopatulika23 Ndamuka ngati mthunzi womka m'tali; ndiingidwa kwina ndi kwina ngati dzombe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Ndamuka ngati mthunzi womka m'tali; ndiingidwa kwina ndi kwina ngati dzombe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Ndazimirira ngati mthunzi wamadzulo, ndapirikitsidwa ngati dzombe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Ndikuzimirira ngati mthunzi wa kumadzulo, ndapirikitsidwa ngati dzombe. Onani mutuwo |