Masalimo 109:24 - Buku Lopatulika24 Mabondo anga agwedezeka chifukwa cha kusala; ndi mnofu wanga waonda posowa mafuta. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Mabondo anga agwedezeka chifukwa cha kusala; ndi mnofu wanga waonda posowa mafuta. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Maondo anga afooka chifukwa chosala zakudya, thupi langa laonda ndi mutu womwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Mawondo anga afowoka chifukwa cha kusala zakudya, thupi langa lawonda ndi mutu wanga womwe. Onani mutuwo |