Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 109:19 - Buku Lopatulika

19 Limkhalire ngati chovala adzikuta nacho, ndi lamba limene adzimangirira nalo m'chuuno chimangirire.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

19 Limkhalire ngati chovala adzikuta nacho, ndi lamba limene adzimangirira nalo m'chuuno chimangirire.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

19 Matemberero akhale ngati mwinjiro wofundira, ngati lamba wovala tsiku ndi tsiku.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

19 Matemberero akhale ngati chofunda chodzikutira nacho, ngati lamba wovala tsiku ndi tsiku.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 109:19
4 Mawu Ofanana  

Anavalanso temberero ngati malaya, ndipo lidamlowa m'kati mwake ngati madzi, ndi ngati mafuta m'mafupa ake.


Otsutsana nane avale manyazi, nadzikute nacho chisokonezo chao ngati ndi chofunda.


Ndidzawaveka adani ake ndi manyazi; koma pa iyeyu korona wake adzamveka.


Achite manyazi, nadodome iwo akukondwera chifukwa cha choipa chidandigwera. Avekeke ndi manyazi ndi kupunzika iwo akudzikuza pa ine.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa