Masalimo 109:20 - Buku Lopatulika20 Ichi chikhale mphotho ya otsutsana nane yowapatsa Yehova, ndi ya iwo akunenera choipa moyo wanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Ichi chikhale mphotho ya otsutsana nane yowapatsa Yehova, ndi ya iwo akunenera choipa moyo wanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Zimenezi zikhale chilango chochokera kwa Chauta kugwera ondineneza. Ziŵagwere amene amalankhula zoipira moyo wanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Awa akhale malipiro ochokera kwa Yehova pa onditsutsa anga, kwa iwo amene amayankhula zoyipa za ine. Onani mutuwo |