Masalimo 109:12 - Buku Lopatulika12 Pasakhale munthu wakumchitira chifundo; kapena kuchitira chokoma ana ake amasiye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Pasakhale munthu wakumchitira chifundo; kapena kuchitira chokoma ana ake amasiye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Pasapezeke ndi mmodzi yemwe womukomera mtima, kapena wina woŵachitira chifundo ana ake amasiye aja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Pasapezeke ndi mmodzi yemwe womukomera mtima kapena kumvera chisoni ana ake amasiye. Onani mutuwo |