Masalimo 108:1 - Buku Lopatulika1 Wakhazikika mtima wanga, Mulungu; ndidzaimba, inde ndidzaimba zolemekeza, ndiko ulemerero wanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Wakhazikika mtima wanga, Mulungu; ndidzaimba, inde ndidzaimba zolemekeza, ndiko ulemerero wanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Inu Mulungu, mtima wanga wakonzeka, ndithu, mtima wanga wakonzekadi! Ndidzaimba nyimbo, nyimbo yake yotamanda. Lumpha, iwe mtima wanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Mtima wanga ndi wokhazikika, Inu Mulungu; ndidzayimba nyimbo, inde ndidzayimba nyimbo zotamanda ndi moyo wanga wonse. Onani mutuwo |