Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 104:8 - Buku Lopatulika

8 anakwera m'mapiri, anatsikira m'zigwa, kufikira malo mudawakonzeratu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 anakwera m'mapiri, anatsikira m'zigwa, kufikira malo mudawakonzeratu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Mapiri adatumphuka, zigwa zidatsika, mpaka kumene Inu mudaakonzeratu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Inu munamiza mapiri, iwo anatsikira ku zigwa kumalo kumene munawakonzera.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 104:8
3 Mawu Ofanana  

Ndipo madzi analinkuchepa kufikira mwezi wakhumi; mwezi wakhumi tsiku loyamba mwezi ndipo padaoneka mitu ya mapiri.


Amaunjika madzi a m'nyanja monga mulu, amakundika zakudya mosungiramo.


Mapiri asanakhazikike, zitunda zisanapangidwe, ndinabadwa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa