Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 104:6 - Buku Lopatulika

6 Mudalikuta ndi nyanja ngati ndi chovala; madzi anafikira pamwamba pa mapiri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Mudalikuta ndi nyanja ngati ndi chovala; madzi anafikira pamwamba pa mapiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Mudaliphimba ndi nyanja yozama ngati ndi chovala, ndipo madzi adakwera mpaka pamwamba pa mapiri.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Munaliphimba ndi nyanja yozama ngati chovala; madzi anayimirira pamwamba pa mapiri.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 104:6
4 Mawu Ofanana  

Ndipo madzi anapambana ndithu padziko lapansi; anamizidwa mapiri aatali onse amene anali pansi pathambo lonse.


Madzi anapambana ndithu nakwera mikono khumi ndi isanu: namizidwa mapiri.


Pakuti ichi aiwala dala, kuti miyamba inakhala kale lomwe, ndi dziko lidaungika ndi madzi ndi mwa madzi, pa mau a Mulungu;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa