Masalimo 104:5 - Buku Lopatulika5 anakhazika dziko lapansi pa maziko ake, silidzagwedezeka kunthawi yonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 anakhazika dziko lapansi pa maziko ake, silidzagwedezeka kunthawi yonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Mudakhazika dziko lapansi pa maziko ake, kuti lisagwedezeke konse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Anakhazikitsa dziko lapansi pa maziko ake; silingasunthike. Onani mutuwo |