Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 104:4 - Buku Lopatulika

4 Amene ayesa mphepo amithenga ake; lawi la moto atumiki ake;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Amene ayesa mphepo amithenga ake; lawi la moto atumiki ake;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Mphepo mumazisandutsa amithenga anu, malaŵi amoto mumaŵasandutsa atumiki anu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Amapanga mphepo kukhala amithenga ake, malawi amoto kukhala atumiki ake.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 104:4
8 Mawu Ofanana  

Ndipo kunachitika, akali chiyendere ndi kukambirana, taonani, anaoneka galeta wamoto ndi akavalo amoto, nawalekanitsa awiriwa; Eliya nakwera kumwamba ndi kamvulumvulu.


Ndipo Elisa anapemphera, nati, Yehova, mumtsegulire maso ake kuti aone. Pamenepo Yehova anamtsegulira maso mnyamatayo, napenya iye, ndipo taonani, paphiripo panadzala ndi akavalo ndi magaleta amoto akumzinga Elisa.


moto ndi matalala, chipale chofewa ndi nkhungu; mphepo ya namondwe, yakuchita mau ake;


Kunena za mafaniziro a zamoyozo, maonekedwe ao ananga makala amoto, monga maonekedwe a miyuni; motowo unayendayenda pakati pa zamoyozo, ndi motowo unachita cheza, ndi m'motomo mudatuluka mphezi.


Ndi mthenga anayankha, nati kwa ine, Izi ndi mphepo zinai zakumwamba zakutuluka kumene zimaimirira pamaso pa Ambuye wa dziko lonse lapansi.


Pakutitu Asaduki anena kuti kulibe kuuka kwa akufa, kapena mngelo, kapena mzimu; koma Afarisi avomereza ponse pawiri.


Kodi siili yonse mizimu yotumikira, yotumidwa kuti itumikire iwo amene adzalowa chipulumutso?


Ndipo za angelo anenadi, Amene ayesa angelo ake mizimu, ndi omtumikira Iye akhale malawi amoto.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa