Masalimo 104:3 - Buku Lopatulika3 Amene alumikiza mitanda ya zipinda zake m'madzi; naika makongwa akhale agaleta ake; nayenda pa mapiko a mphepo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Amene alumikiza mitanda ya zipinda zake m'madzi; naika makongwa akhale agaleta ake; nayenda pa mapiko a mphepo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Mwamanga Nyumba yanu pa madzi akumwamba, mitambo yaliŵiro ili ngati galeta lanu, mumayenda pa mapiko a mphepo, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 ndipo wayika pa madzi mitanda ya chipinda chake. Iye amasandutsa mitambo kukhala galeta lake, ndi kuwuluka pa mapiko a mphepo. Onani mutuwo |