Masalimo 104:12 - Buku Lopatulika12 Mbalame za mlengalenga zifatsa pamenepo, zimaimba pakati pa mitawi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Mbalame za mlengalenga zifatsa pamenepo, zimaimba pakati pa mitawi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Mbalame zimamanga zisa pafupi ndi mitsinjeyo, zimaimba m'nthambi za mitengo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Mbalame zamlengalenga zimayika zisa mʼmbali mwa madzi; zimayimba pakati pa thambo. Onani mutuwo |