Masalimo 104:13 - Buku Lopatulika13 Iye amwetsa mapiri mochokera m'zipinda zake: Dziko lakhuta zipatso za ntchito zanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Iye amwetsa mapiri mochokera m'zipinda zake: Dziko lakhuta zipatso za ntchito zanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Inu mumathirira mapiri ndi madzi ochokera ku malo anu akumwamba. Dziko lapansi ladzaza ndi madalitso anu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Iye amathirira mapiri kuchokera ku zipinda zake zapamwamba; dziko lapansi limakhutitsidwa ndi chipatso cha ntchito yake. Onani mutuwo |