Masalimo 103:9 - Buku Lopatulika9 Sadzatsutsana nao nthawi zonse; ndipo sadzasunga mkwiyo wake kosatha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Sadzatsutsana nao nthawi zonse; ndipo sadzasunga mkwiyo wake kosatha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Akatikalipira, mkwiyo wake sudzakhala woyaka mpakampaka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Iye sadzatsutsa nthawi zonse, kapena kusunga mkwiyo wake kwamuyaya; Onani mutuwo |