Masalimo 103:10 - Buku Lopatulika10 Sanatichitira monga mwa zolakwa zathu, kapena kutibwezera monga mwa mphulupulu zathu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Sanatichitira monga mwa zolakwa zathu, kapena kutibwezera monga mwa mphulupulu zathu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Satilanga moyenerera machimo athu, satibwezera molingana ndi zolakwa zathu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 satichitira molingana ndi machimo athu, kapena kutibwezera molingana ndi mphulupulu zathu. Onani mutuwo |