Masalimo 103:8 - Buku Lopatulika8 Yehova ndiye wa nsoni zokoma ndi wachisomo, wosakwiya msanga, ndi wa chifundo chochuluka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Yehova ndiye wa nsoni zokoma ndi wachisomo, wosakwiya msanga, ndi wa chifundo chochuluka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Chauta ndi wachifundo ndi wokoma mtima, ndi wosakwiya msanga, ndipo chikondi chake chosasinthika nchachikulu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Yehova ndi wachifundo ndi wokoma mtima, wosakwiya msanga ndi wachikondi chochuluka. Onani mutuwo |