Masalimo 10:4 - Buku Lopatulika4 Woipa, monga mwa kudzikuza kwa nkhope yake, akuti, Sadzafunsira. Malingaliro ake onse akuti, Palibe Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Woipa, monga mwa kudzikuza kwa nkhope yake, akuti, Sadzafunsira. Malingaliro ake onse akuti, Palibe Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Munthu woipa sasamala Mulungu chifukwa cha kunyada kwake. Mumtima mwake amati, “Kulibe Mulungu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Mwa kunyada kwake woyipa safunafuna Mulungu; mʼmaganizo ake wonse mulibe malo a Mulungu. Onani mutuwo |