Masalimo 10:3 - Buku Lopatulika3 Pakuti woipa adzitamira chifuniro cha moyo wake, adalitsa wosirira, koma anyoza Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Pakuti woipa adzitamira chifuniro cha moyo wake, adalitsa wosirira, koma anyoza Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Paja munthu woipa amanyadira zokhumba za mtima wake, wokonda chuma amanyoza ndi kukana Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Iye amatamandira zokhumba za mu mtima wake; amadalitsa aumbombo ndi kuchitira chipongwe Yehova. Onani mutuwo |