Masalimo 10:18 - Buku Lopatulika18 kuti muweruze mlandu wa amasiye ndi wokhalira mphanthi, kuti munthu wa padziko lapansi angaonjeze kuopsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 kuti muweruze mlandu wa amasiye ndi wokhalira mphanthi, kuti munthu wa pa dziko lapansi angaonjeze kuopsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Potero mudzaŵateteza amasiye ndi opsinjidwa, kuti anthu amene ali a pansi pano, asadzathe kuwopsezanso. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Kuteteza ana amasiye ndi oponderezedwa, ndi cholinga chakuti munthu amene ali wa dziko lapansi asaopsenso. Onani mutuwo |