Masalimo 10:17 - Buku Lopatulika17 Yehova, mwamva chikhumbo cha ozunzika, mudzakhazikitsa mtima wao, mudzatchereza khutu lanu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Yehova, mwamva chikhumbo cha ozunzika, mudzakhazikitsa mtima wao, mudzatchereza khutu lanu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Chauta, mumamva zimene odzichepetsa amapempha. Mudzalimbitsa mitima yao, mudzaŵatchera khutu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Mumamva Inu Yehova, zokhumba za osautsidwa; mumawalimbikitsa ndipo mumamva kulira kwawo. Onani mutuwo |