Masalimo 10:16 - Buku Lopatulika16 Yehova ndiye Mfumu kunthawi yamuyaya; aonongeka amitundu m'dziko lake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Yehova ndiye Mfumu kunthawi yamuyaya; aonongeka amitundu m'dziko lake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Chauta ndiye Mfumu mpaka muyaya. Mitundu ya anthu akunja idzatheratu m'dziko lake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Yehova ndi Mfumu kwamuyaya; mitundu ya anthu idzawonongeka kuchoka mʼdziko lake. Onani mutuwo |