Marko 9:23 - Buku Lopatulika23 Ndipo Yesu ananena naye, Ngati mukhoza! Zinthu zonse zitheka ndi iye wakukhulupirira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Ndipo Yesu ananena naye, Ngati mukhoza! Zinthu zonse zitheka ndi iye wakukhulupirira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Yesu adati, “Bwanji mukuti, ‘Ngati mungathe?’ Zinthu zonse nzotheka kwa amene ali ndi chikhulupiriro.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Yesu anati, “ ‘Ngati mungathe!’ Zinthu zonse ndi zotheka kwa iye amene akhulupirira.” Onani mutuwo |