Marko 9:24 - Buku Lopatulika24 Pomwepo atate wa mwana anafuula, nanena, Ndikhulupirira; thandizani kusakhulupirira kwanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Pomwepo atate wa mwana anafuula, nanena, Ndikhulupirira; thandizani kusakhulupirira kwanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Pomwepo bambo wa mwana uja adanena mokweza mau kuti, “Ndikukhulupirira, koma mpang'ono chabe. Thandizeni kuti ndikhulupirire kwenikweni.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Nthawi yomweyo abambo a mwanayo anafuwula kuti, “Ndikhulupirira; thandizani kusakhulupirira kwanga!” Onani mutuwo |