Marko 9:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo Iye ananena nao, Eliya ayamba kudza ndithu, nadzakonza zinthu zonse; ndipo kwalembedwa bwanji za Mwana wa Munthu, kuti ayenera kumva zowawa zambiri ndi kuyesedwa chabe? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo Iye ananena nao, Eliya ayamba kudza ndithu, nadzakonza zinthu zonse; ndipo kwalembedwa bwanji za Mwana wa Munthu, kuti ayenera kumva zowawa zambiri ndi kuyesedwa chabe? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Yesu adaŵayankha kuti, “Zoonadi, Eliya adzayambadi wabwera, kuti adzakonzenso zonse. Komabe bwanji Malembo amanena kuti Mwana wa Munthu adzayenera kuzunzidwa kwambiri ndi kunyozedwa? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Yesu anayankha kuti, “Kunena motsimikiza, Eliya ayeneradi kuyamba kubwera kudzakonzanso zinthu zonse. Nʼchifukwa chiyani tsono zinalembedwa, kuti Mwana wa Munthu ayenera kuvutika kwambiri ndi kukanidwa? Onani mutuwo |