Marko 9:13 - Buku Lopatulika13 Koma ndinena ndi inu kuti anafikadi Eliya, ndipo anamchitiranso zilizonse iwo anazifuna, monga kwalembedwa za iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Koma ndinena ndi inu kuti anafikadi Eliya, ndipo anamchitiranso zilizonse iwo anazifuna, monga kwalembedwa za iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Ine ndikukuuzani kuti Eliya adafikadi, ndipo anthu adamchita zonse zomwe iwo ankafuna, monga momwe Malembo adaanenera za iye.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Koma ndikuwuzani, kuti Eliya wabweradi, ndipo amuchitira iye zonse zimene iwo anafuna, monga momwe zalembedwera za iye.” Onani mutuwo |