Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 8:9 - Buku Lopatulika

9 Ndipo iwo anali ngati zikwi zinai; ndipo Iye analawirana nao.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Ndipo iwo anali ngati zikwi zinai; ndipo Iye analawirana nao.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Anthu amene adaali pamenepo, amuna okha adaalipo ngati zikwi zinai.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Panali amuna pafupifupi 4,000. Ndipo atawawuza kuti apite kwawo,

Onani mutuwo Koperani




Marko 8:9
4 Mawu Ofanana  

Pomwepo Iye anasiya makamuwo, nalowa m'nyumba; ndimo ophunzira ake anadza kwa Iye, nanena, Mutitanthauzire fanizo lija la namsongole wa m'munda.


Ndipo pomwepo analowa m'ngalawa ndi ophunzira ake, nafika ku mbali ya ku Dalamanuta.


Ndipo anadya nakhuta; ndipo anatola makombo madengu asanu ndi awiri.


Ndipo anadzitengera khumi ndi awiriwo, nati kwa iwo, Taonani, tikwera kunka ku Yerusalemu, ndipo zidzakwaniritsidwa kwa Mwana wa Munthu zonse zolembedwa ndi aneneri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa