Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 8:8 - Buku Lopatulika

8 Ndipo anadya nakhuta; ndipo anatola makombo madengu asanu ndi awiri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Ndipo anadya nakhuta; ndipo anatola makombo madengu asanu ndi awiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Anthu adadya mpaka kukhuta. Adatola zotsala, nadzaza madengu asanu ndi aŵiri.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Anthu anadya ndipo anakhuta. Atamaliza, ophunzira anatola buledi ndi nsomba zotsalira ndi kudzaza madengu asanu ndi awiri.

Onani mutuwo Koperani




Marko 8:8
16 Mawu Ofanana  

Muolowetsa dzanja lanu, nimukwaniritsira zamoyo zonse chokhumba chao.


Ndipo anadya onse, nakhuta; ndipo anatola makombo otsala, nadzala madengu khumi ndi iwiri.


Ndipo onsewa anadya, nakhuta: ndipo anatola makombo otsala madengu asanu ndi awiri odzala.


Penanso mikate isanu ndi iwiri ija ya anthu zikwi zinai, ndi madengu angati munawatola?


Ndipo iwo anali ngati zikwi zinai; ndipo Iye analawirana nao.


Anawakhutitsa anjala ndi zinthu zabwino, ndipo eni chuma anawachotsa opanda kanthu.


Gwirani ntchito si chifukwa cha chakudya chimene chitayika koma cha chakudya chimene chitsalira kumoyo wosatha, chimene Mwana wa Munthu adzakupatsani inu; pakuti ameneyo Atate, ndiye Mulungu, adamlembera chizindikiro.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa