Marko 8:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo ophunzira ake anamyankha Iye, kuti, Munthu adzatha kutenga kuti mikate yakukhutitsa anthu awa m'chipululu muno? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo ophunzira ake anamyankha Iye, kuti, Munthu adzatha kutenga kuti mikate yakukhutitsa anthu awa m'chipululu muno? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Ophunzira ake adamufunsa kuti, “Anthu ochuluka chotereŵa munthu angaŵapezere bwanji chakudya chokwanira, kuthengo ngati kuno?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Ophunzira ake anayankha nati, “Kodi ndi kuti kuthengo kuno kumene munthu angapeze buledi okwanira kuwadyetsa?” Onani mutuwo |