Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 8:26 - Buku Lopatulika

26 Ndipo anamtumiza amuke kwao, nanena, Usalowe konse m'mudzi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

26 Ndipo anamtumiza amuke kwao, nanena, Usalowe konse m'mudzi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

26 Yesu adamuuza kuti apite kwao, namlamula kuti, “Usaloŵe ndi m'mudzi momwemu.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

26 Yesu anamuwuza kuti apite kwawo nati, “Usapite mʼmudzimo.”

Onani mutuwo Koperani




Marko 8:26
7 Mawu Ofanana  

nawalimbitsira mau kuti asamuwulule Iye;


Ndipo Yesu ananena naye, Ona, iwe, usauze munthu; koma muka, udzionetse wekha kwa wansembe, nupereke mtulo umene anaulamulira Mose, ukhale mboni kwa iwo.


Ndipo maso ao anaphenyuka. Ndipo Yesu anawauzitsa iwo, nanena, Yang'anirani, asadziwe munthu aliyense.


Ndipo anawalamulira kwambiri kuti asadziwe ichi munthu mmodzi, nawauza kuti ampatse iye kudya.


Ndipo anawalamulira kuti asauze munthu aliyense; koma monga momwe Iye anawalamulitsa momwenso makamaka analalikira kopambana.


Ndipo anamgwira dzanja munthu wakhunguyo, natulukira naye kunja kwa mudzi; ndipo atamthira malovu m'maso mwake, naika manja pa iye, anamfunsa, Uona kanthu kodi?


Pamenepo anaikanso manja m'maso mwake; ndipo anapenyetsa, nachiritsidwa, naona zonse mbee.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa