Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 8:27 - Buku Lopatulika

27 Ndipo anatuluka Yesu, ndi ophunzira ake, nalowa kumidzi ya ku Kesareya-Filipi; ndipo panjira anafunsa ophunzira ake, nanena nao, Kodi anthu ananena kuti Ine ndine yani?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

27 Ndipo anatuluka Yesu, ndi ophunzira ake, nalowa kumidzi ya ku Kesareya-Filipi; ndipo panjira anafunsa ophunzira ake, nanena nao, Kodi anthu ananena kuti Ine ndine yani?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

27 Yesu ndi ophunzira ake adapita ku midzi ya ku Kesareya-Filipi. Pa njira Yesu adafunsa ophunzira akewo kuti, “Kodi anthu amati Ine ndine yani?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

27 Yesu ndi ophunzira ake anapita ku midzi yozungulira Kaisareya wa Filipo. Ali panjira, Iye anawafunsa kuti, “Kodi anthu amati ndine yani?”

Onani mutuwo Koperani




Marko 8:27
2 Mawu Ofanana  

Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa