Marko 8:13 - Buku Lopatulika13 Ndipo anawasiya iwo, nalowanso m'ngalawa, nachoka kunka ku tsidya lija. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndipo anawasiya iwo, nalowanso m'ngalawa, nachoka kunka ku tsidya lija. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Atatero, Yesu adaŵasiya, naloŵanso m'chombo kuwolokera ku tsidya lina. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Ndipo anawasiya, nalowanso mʼbwato ndi kuwolokera tsidya lina. Onani mutuwo |