Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 8:14 - Buku Lopatulika

14 Ndipo ophunzira adaiwala kutenga mikate, ndipo analibe mkate m'ngalawa koma umodzi wokha.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

14 Ndipo ophunzira adaiwala kutenga mikate, ndipo analibe mkate m'ngalawa koma umodzi wokha.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

14 Ophunzira a Yesu anali ataiŵala kutenga buledi, kotero kuti m'chombomo adaali ndi buledi mmodzi yekha.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

14 Ophunzira anayiwala kutenga buledi, kupatula buledi mmodzi yekha amene anali naye mʼbwato.

Onani mutuwo Koperani




Marko 8:14
3 Mawu Ofanana  

Ndipo ophunzira anadza kutsidya linalo, naiwala kutenga mikate.


Ndipo anawasiya iwo, nalowanso m'ngalawa, nachoka kunka ku tsidya lija.


Ndipo Iye anawalamula, nanena, Yang'anirani, penyani kuti mupewe chotupitsa mkate cha Afarisi, ndi chotupitsa mkate cha Herode.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa