Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 7:8 - Buku Lopatulika

8 Musiya lamulo la Mulungu, nimusunga mwambo wa anthu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Musiya lamulo la Mulungu, nimusunga mwambo wa anthu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Kenaka Yesu adati, “Inu mumasiya Malamulo a Mulungu, nkumasunga miyambo ya anthu.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Mwasiya malamulo a Mulungu ndipo mwagwiritsitsa miyambo ya anthu.”

Onani mutuwo Koperani




Marko 7:8
4 Mawu Ofanana  

Pakudzaonekera inu pamaso pa Ine, ndani wafuna chimenechi m'dzanja lanu, kupondaponda m'mabwalo mwanga?


Ndipo Afarisi ndi alembi anamfunsa Iye, kuti, Bwanji ophunzira anu satsata mwambo wa akulu, koma akudya mkate wao ndi m'manja mwakuda?


ndipo ndinawaposa ndi kutsogola mwa Chiyuda ambiri a msinkhu wanga mwa mtundu wanga, ndipo ndinakhala wachangu koposa pa miyambo ya makolo anga.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa