Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 7:30 - Buku Lopatulika

30 Ndipo anachoka kunka kunyumba kwake, napeza mwana atamgoneka pakama, ndi chiwanda chitatuluka.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

30 Ndipo anachoka kunka kunyumba kwake, napeza mwana atamgoneka pakama, ndi chiwanda chitatuluka.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

30 Mai uja adabwerera kunyumba kwake, nakapezadi mwanayo ali gone pa bedi, mzimu woipa uja utatuluka.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

30 Atapita kwawo anakapeza mwana wake aligone pa bedi, chiwanda chitatuluka.

Onani mutuwo Koperani




Marko 7:30
4 Mawu Ofanana  

Ndipo anati kwa iye, Chifukwa cha mau amene, muka; chiwanda chatuluka m'mwana wako wamkazi.


Ndipo anatulukanso m'maiko a ku Tiro, nadzera pakati pa Sidoni, kufikira ku nyanja ya Galileya, ndi kupyola pakati pa maiko a ku Dekapoli.


iye wochita tchimo ali wochokera mwa mdierekezi, chifukwa mdierekezi amachimwa kuyambira pachiyambi. Kukachita ichi Mwana wa Mulungu adaonekera, ndiko kuti akaononge ntchito za mdierekezi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa