Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 7:29 - Buku Lopatulika

29 Ndipo anati kwa iye, Chifukwa cha mau amene, muka; chiwanda chatuluka m'mwana wako wamkazi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

29 Ndipo anati kwa iye, Chifukwa cha mau amene, muka; chiwanda chatuluka m'mwana wako wamkazi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

29 Apo Yesu adamuuza kuti, “Chifukwa cha mau mwanenaŵa, pitani, mzimu woipawo watuluka mwa mwana wanu.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

29 Ndipo Iye anamuwuza kuti, “Chifukwa cha yankholi, ukhoza kupita; chiwanda chachoka mwa mwana wako wamkazi.”

Onani mutuwo Koperani




Marko 7:29
7 Mawu Ofanana  

Pakuti zonsezi mkono wanga wazilenga, momwemo zonsezi zinaoneka, ati Yehova; koma ndidzayang'anira munthu uyu amene ali waumphawi, ndi wa mzimu wosweka, nanthunthumira ndi mau anga.


Odala ali osauka mumzimu; chifukwa uli wao Ufumu wa Kumwamba.


Koma iye anavomera nanena ndi Iye, Inde Ambuye; tingakhale tiagalu ta pansi pa gome tikudyako nyenyeswa za ana.


Ndipo anachoka kunka kunyumba kwake, napeza mwana atamgoneka pakama, ndi chiwanda chitatuluka.


iye wochita tchimo ali wochokera mwa mdierekezi, chifukwa mdierekezi amachimwa kuyambira pachiyambi. Kukachita ichi Mwana wa Mulungu adaonekera, ndiko kuti akaononge ntchito za mdierekezi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa