Marko 7:2 - Buku Lopatulika2 ndipo anaona kuti ophunzira ake ena anadya mkate ndi m'manja mwakuda, ndiwo osasamba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 ndipo anaona kuti ophunzira ake ena anadya mkate ndi m'manja mwakuda, ndiwo osasamba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Iwo adaaona kuti ophunzira ake ena ankangodya chakudya osasamba m'manja moyenera (ndiye kuti mosasamala mwambo wosamba m'manja.) Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 iwo anaona ophunzira ake akudya chakudya ndi mʼmanja mwakuda kapena kuti mʼmanja mosasamba. Onani mutuwo |