Marko 7:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo anasonkhana kwa Iye Afarisi, ndi alembi ena, akuchokera ku Yerusalemu, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo anasonkhana kwa Iye Afarisi, ndi alembi ena, akuchokera ku Yerusalemu, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Tsiku lina Afarisi ena pamodzi ndi aphunzitsi ena a Malamulo, amene adaachokera ku Yerusalemu, adasonkhana kwa Yesu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Afarisi ndi ena mwa aphunzitsi amalamulo omwe anachokera ku Yerusalemu anasonkhana momuzungulira Yesu ndipo Onani mutuwo |