Marko 7:13 - Buku Lopatulika13 muyesa achabe mau a Mulungu mwa mwambo wanu, umene munaupereka: ndi zinthu zotere zambiri muzichita. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 muyesa achabe mau a Mulungu mwa mwambo wanu, umene munaupereka: ndi zinthu zotere zambiri muzichita. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Pakutero mau a Mulungu inu mumaŵasandutsa achabechabe, chifukwa cha mwambo wanu umene mumasiyirana. Ndipo mumachita zinanso zambiri zotere.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Potero mumachepetsa mawu a Mulungu kukhala wopanda mphamvu ndi miyambo yanu imene mumapatsirana. Ndipo mumachita zinthu zina zambiri monga zimenezi.” Onani mutuwo |