Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 6:9 - Buku Lopatulika

9 koma avale nsapato; ndipo anati, Musavale malaya awiri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 koma avale nsapato; ndipo anati, Musavale malaya awiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Nsapato muvale inde, koma musakhale ndi mikanjo iŵiri.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Muvale nsapato koma osatenga malaya apadera.

Onani mutuwo Koperani




Marko 6:9
6 Mawu Ofanana  

kapena thumba la kamba la kunjira, kapena malaya awiri, kapena nsapato, kapena ndodo; pakuti wantchito ayenera kulandira zakudya zake.


Inetu ndikubatizani inu ndi madzi kuloza ku kutembenuka mtima; koma Iye wakudza pambuyo panga, ali wakundiposa mphamvu, amene sindiyenera kunyamula nsapato zake: Iyeyu adzakubatizani inu ndi Mzimu Woyera ndi moto:


Ndipo ananena nao, Kumene kulikonse mukalowa m'nyumba, khalani komweko kufikira mukachokako.


ndipo anawauza kuti asatenge kanthu ka paulendo, koma ndodo yokha; asatenge mkate, kapena thumba, kapena ndalama m'lamba lao;


Ndipo mngelo anati kwa iye, Dzimangire m'chuuno, numange nsapato zako. Nachita chotero. Ndipo ananena naye, Funda chovala chako, nunditsate ine.


ndipo mutadziveka mapazi anu ndi makonzedwe a Uthenga Wabwino wa mtendere;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa