Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 6:10 - Buku Lopatulika

10 Ndipo ananena nao, Kumene kulikonse mukalowa m'nyumba, khalani komweko kufikira mukachokako.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Ndipo ananena nao, Kumene kulikonse mukalowa m'nyumba, khalani komweko kufikira mukachokako.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Adaŵauzanso kuti, “Mukafika pa mudzi, muzikhala nao kunyumba kumene mudafikirako, mpaka itakwana nthaŵi yoti muchoke kumudziko.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Pamene mulowa mʼnyumba mukakhale momwemo kufikira mutachoka mʼmudzimo.

Onani mutuwo Koperani




Marko 6:10
7 Mawu Ofanana  

Ndipo pamalo ponse sakulandirani, kapena kumvera inu, pakuchoka kumeneko, sansani fumbi lili kumapazi anu, likhale mboni ya kwa iwo.


koma avale nsapato; ndipo anati, Musavale malaya awiri.


Ndipo m'nyumba iliyonse mukalowemo, khalani komweko, ndipo muzikachokera kumeneko.


Pamene anabatizidwa iye ndi a pabanja pake anatidandaulira ife, kuti, Ngati mwandiyesera ine wokhulupirika kwa Ambuye, mulowe m'nyumba yanga, mugone m'menemo. Ndipo anatiumiriza ife.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa